Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 40:27 - Buku Lopatulika

nafukizapo chofukiza cha fungo lokoma; monga Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nafukizapo chofukiza cha fungo lokoma; monga Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adafukiza lubani wa fungo lokoma paguwapo, monga momwe Chauta adamlamulira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo anapserezapo lubani wonunkhira monga Yehova anamulamulira.

Onani mutuwo



Eksodo 40:27
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Aroni azifukizapo chofukiza cha zonunkhira zokoma m'mawa ndi m'mawa, pamene akonza nyalizo, achifukize.


Ndipo anapachika pa chihema nsalu yotsekera pakhomo.