Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 4:26 - Buku Lopatulika

Pamenepo anati mkaziyo, Mkwati wamwazi iwe, chifukwa cha mdulidwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo anati mkaziyo, Mkwati wamwazi iwe, chifukwa cha mdulidwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Chauta adamleka Mose osamupha. Ndiye pamene Zipora adanena kuti, “Ndiwe mkwati woomboledwa ndi magazi,” chifukwa cha kuumbalako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Yehova anamuleka Mose wosamupha. Pa nthawiyo, Zipora anati, “Mkwati wa magazi,” ponena za mdulidwe.

Onani mutuwo



Eksodo 4:26
2 Mawu Ofanana  

Koma Zipora anatenga mpeni wamwala, nadula khungu la mwana wake, naliponya pa mapazi ake; nati, Pakuti iwe ndiwe mkwati wanga wamwazi. Ndipo Iye anamleka.


Ndipo Yehova ananena ndi Aroni, Muka kuchipululu kukakomana ndi Mose. Ndipo anamuka, nakomana naye paphiri la Mulungu, nampsompsona.