Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 39:12 - Buku Lopatulika

Ndi mzere wachitatu wa lesemu, sibu, ndi akalama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi mzere wachitatu wa lesemu, sibu, ndi akalama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mzere wachitatu adaika miyala ya opela, agate ndi ametisiti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mzere wachitatu anayikapo miyala ya opera, agate ndi ametisiti;

Onani mutuwo



Eksodo 39:12
3 Mawu Ofanana  

ndi mzere wachitatu wa lesemu, sibu, ndi akalama;


Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.


Ndi mzere wachinai wa tarisisi, sohamu, ndi yasefe; inakhala yogwirika ndi golide maikidwe ake.