Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 39:11 - Buku Lopatulika

Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mzere wachiŵiri adaika miyala ya emeradi, safiro ndi daimondi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mzere wachiwiri anayikapo miyala ya emeradi, safiro ndi dayimondi;

Onani mutuwo



Eksodo 39:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uikepo miyala yoikikapo, mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba;


ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahaloni;


Ndipo anaika pomwepo mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba.


Ndi mzere wachitatu wa lesemu, sibu, ndi akalama.


Unali mu Edeni, munda wa Mulungu, mwala uliwonse wa mtengo wake unali chofunda chako, sardiyo, topazi, diamondi, berulo, sohamu, ndi yaspi, safiro, nofeki, bareketi, ndi golide; malingaka ako ndi akazi ako anakutumikira tsiku lolengedwa iwe zinakonzekeratu.