Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 28:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo uikepo miyala yoikikapo, mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo uikepo miyala yoikikapo, mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Usokererepo mizere inai ya miyala. Pa mzere woyamba pakhale miyala ya rubi, topazi ndi garaneti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Uyikepo mizere inayi ya miyala yokongola kwambiri. Mzere woyamba ukhale ndi miyala ya rubi, topazi ndi berili.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 28:17
15 Mawu Ofanana  

Uloche miyala iwiriyo ndi maina a ana a Israele, monga mwa ntchito ya wolocha miyala, monga malembedwe a chosindikizira, uipange igwirike ndi zoikamo zagolide.


Chikhale chaphwamphwa, chopindika, utali wake dzanja limodzi, ndi kupingasa kwake dzanja limodzi.


ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahaloni;


Ndipo utenge miyala iwiri yaberulo, nulochepo maina a ana a Israele;


Alipo golide ndi ngale zambiri; koma milomo yodziwa ndiyo chokometsera cha mtengo wapatali.


Mtengo wake uposa ngale; ndipo zonse zikukondweretsa sizilingana naye.


Mkazi wangwiro ndani angampeze? Pakuti mtengo wake uposa ngale.


Pakuti nzeru iposa ngale, ndi zonse tizifunitsa sizilingana nayo.


Omveka ake anakonzeka koposa chipale chofewa, nayera koposa mkaka, matupi ao anafiira koposa timiyala toti psu; maonekedwe ao ananga a safiro wa mtengo wapatali.


Unali mu Edeni, munda wa Mulungu, mwala uliwonse wa mtengo wake unali chofunda chako, sardiyo, topazi, diamondi, berulo, sohamu, ndi yaspi, safiro, nofeki, bareketi, ndi golide; malingaka ako ndi akazi ako anakutumikira tsiku lolengedwa iwe zinakonzekeratu.


Ndipo adzakhala angaanga, ati Yehova wa makamu, tsiku ndidzaikalo, ndipo ndidzawaleka monga munthu aleka mwana wake womtumikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa