Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 31:5 - Buku Lopatulika

ndi kuzokota miyala yoikika, ndi kozokota mtengo, kuchita ntchito zilizonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi kuzokota miyala yoikika, ndi kozokota mtengo, kuchita ntchito zilizonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akudziŵanso kuzokota miyala yogwira nayo ntchito, kujoba mitengo, ndi kuchita zaluso zonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kusema ndi kuyika miyala yokongola, kukonza zinthu zamatabwa ndiponso kugwira ntchito ina iliyonse yamanja.

Onani mutuwo



Eksodo 31:5
4 Mawu Ofanana  

Koma ali nayo mphamvu ndani yakummangira Iye nyumba, popeza thambo lam'mwambamwamba silimfikira? Ndine yani ine tsono, kuti ndimmangire nyumba, koma kumfukizira chofukiza ndiko?


kulingirira ntchito zaluso, kuchita ndi golide ndi siliva ndi mkuwa,


Ndipo Ine, taona, ndampatsa Oholiyabu, mwana wa Ahisamaki, wa fuko la Dani, akhale naye; ndipo ndaika luso m'mitima ya onse a mtima waluso, kuti apange zonse ndakuuza iwe;