Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 28:13 - Buku Lopatulika

Ndipo upange zoikamo za golide;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo upange zoikamo za golide;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Upangenso zoikamo zonga maluŵa agolide,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upange zoyikamo za maluwa agolide,

Onani mutuwo



Eksodo 28:13
4 Mawu Ofanana  

Uloche miyala iwiriyo ndi maina a ana a Israele, monga mwa ntchito ya wolocha miyala, monga malembedwe a chosindikizira, uipange igwirike ndi zoikamo zagolide.


ndi maunyolo awiri a golide woona; uwapote ngati zingwe, ntchito yopota; numange maunyolo opotawo pazoikamo.


Anapanganso zoikamo ziwiri zagolide, ndi mphete ziwiri zagolide; naika mphete ziwirizo pansonga ziwiri za chapachifuwa.


Ndipo anaomba chapachifuwa, ntchito ya mmisiri, monga maombedwe ake a efodi; cha golide, lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa.