Eksodo 28:14 - Buku Lopatulika14 ndi maunyolo awiri a golide woona; uwapote ngati zingwe, ntchito yopota; numange maunyolo opotawo pazoikamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 ndi maunyolo awiri a golide woona; uwapote ngati zingwe, ntchito yopota; numange maunyolo opotawo pazoikamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 ndiponso maunyolo aŵiri a golide wokoma, opotedwa ngati zingwe, amene udzaŵalumikize ku zoikamozo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 ndiponso maunyolo awiri a golide wabwino kwambiri, wopetedwa ngati zingwe ndipo uwalumikize ku zoyikamozo. Onani mutuwo |