Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:23 - Buku Lopatulika

Nupange matabwa awiri angodya za chihema cha kumbuyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nupange matabwa awiri angodya za Kachisi za kumbuyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumbuyo kwa chihema konko, pangodya pakhale mafulemu aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo upangenso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.

Onani mutuwo



Eksodo 26:23
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anadulitsa ndi matabwa amkungudza mikono makumi awiri m'kati mwa nyumba m'tsogolo mwake, kuyambira pansi kulekeza kumitanda; ichi anamanga kukhala chipinda chamkati, malo opatulika kwambiri.


Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya chihema cha kumbuyo.


Ndipo akhale ophatikizika pamodzi patsinde, nakhalenso ophatikizika pamodzi kumutu kwake ndi mphete imodzi; azitero onse awiri; azikhala angodya ziwiri.