Eksodo 26:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo upangenso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti. Onani mutuwoBuku Lopatulika23 Nupange matabwa awiri angodya za chihema cha kumbuyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Nupange matabwa awiri angodya za Kachisi za kumbuyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Kumbuyo kwa chihema konko, pangodya pakhale mafulemu aŵiri. Onani mutuwo |