Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:18 - Buku Lopatulika

Ndipo uzipanga matabwa a chihema, matabwa makumi awiri ku mbali ya kumwera, kumwera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo uzipanga matabwa a Kachisi, matabwa makumi awiri ku mbali ya kumwera, kumwera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Popanga mafulemuwo, ku mbali yakumwera, upange makumi aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upange maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho.

Onani mutuwo



Eksodo 26:18
4 Mawu Ofanana  

Maziko ake anakumbidwa pa chiyani? Kapena anaika ndani mwala wake wa pangodya,


Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


Pa thabwa limodzi pakhale mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; uzitero pa matabwa onse a chihema.


Nuzipanga makamwa makumi anai asiliva pansi pa matabwa makumi awiri; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi kwa mitsukwa yake iwiri, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina kwa mitsukwa yake iwiri;