Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:12 - Buku Lopatulika

Ndipo chotsalacho pansalu yophimbayo, hafu yake ya nsalu yotsalirayo, itchinge pambuyo pake pa chihemacho.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo chotsalacho pa nsalu za hemalo, hafu yake ya nsalu yotsalirayo, ichinge pambuyo pake pa Kachisi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Theka la nsalu yotsalira ija idzalendeŵera kumbuyo kwa chihemacho.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Theka lotsalira la nsaluyo lidzalendewera kumbuyo kwa chihemacho.

Onani mutuwo



Eksodo 26:12
3 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga zokowera makumi asanu zamkuwa, ndi kukowetsa zokowerazo m'magangomo, ndi kumanga pamodzi hemalo likhale limodzi.


Ndi mkono wa pa mbali ino, ndi mkono wa pa mbali inzake, wakutsalira mu utali wake wa nsalu zophimbazo, itchinge pambali zake za chihemacho, mbali ino ndi mbali ina, kumphimba.


Ndipo uziomba nsalu zophimba za ubweya wa mbuzi zikhale chophimba pamwamba pa chihema; uziomba nsalu khumi ndi imodzi.