Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:3 - Buku Lopatulika

Ndipo choperekacho uchilandire kwa iwo ndi ichi: golide, ndi siliva, ndi mkuwa,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo choperekacho uchilandire kwa iwo ndi ichi: golide, ndi siliva, ndi mkuwa,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zopereka zimene ulandirezo ndi izi: golide, siliva, mkuŵa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zopereka zimene ulandire kwa anthuwo ndi izi: Golide, siliva ndi mkuwa.

Onani mutuwo



Eksodo 25:3
5 Mawu Ofanana  

Chitsulo achitenga m'nthaka, ndi mkuwa ausungunula kumwala.


Lankhula ndi ana a Israele, kuti anditengere chopereka; ulandire chopereka changa kwa munthu aliyense mtima wake umfunitsa mwini.


ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi;


Ndipo atenge golide, ndi lamadzi ndi lofiirira ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa.


dziko loti mudzadyamo mkate wosapereweza; simudzasowamo kanthu; dziko loti miyala yake nja chitsulo, ndi m'mapiri ake mukumbe mkuwa.