Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 22:12 - Buku Lopatulika

Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati chidabedwa kwaoko ndithu, alipe kwa mwiniyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ngati choŵetacho chidabedwa, mwiniwakeyo adzalipidwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati chiwetocho chinabedwa, iye ayenera kubwezera mwini wakeyo.

Onani mutuwo



Eksodo 22:12
4 Mawu Ofanana  

Chimene chinazomoledwa ndi chilombo sindinachitengere kwa iwe; ndekha ndinalipira; padzanja langa unachifuna, chingakhale chobedwa kapena pausiku kapena pausana.


lumbiro la Yehova likhale pakati pa iwo awiri, kuti sanatulutse dzanja lake pa chuma cha mnansi wake; ndipo mwiniyo azivomereza, ndipo asalipe.


Ngati chajiwa ndithu, abwere nacho chikhale mboni; asalipe pa chojiwacho.


Munthu akaikiza ndalama kapena chuma kwa mnansi wake, ndipo zibedwa m'nyumba ya munthuyo; akapeza mbala, ilipe chowirikiza.