Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:9 - Buku Lopatulika

Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana aakazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana akazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akaganiza zopatsa mwana wake mkaziyo, azidzamsunga ngati mwana wake wamkazi ndithu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati anamusankha kuti akhale mkazi wa mwana wake, ayenera kumusunga ngati mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo



Eksodo 21:9
2 Mawu Ofanana  

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.


Akapanda kumkonda mbuye wake, amene anamtoma mwini yekha, azilola kuti amuombole; alibe mphamvu yakumgulitsa kwa anthu achilendo, popeza wachita naye monyenga.