Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:10 - Buku Lopatulika

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akakwatira mkazi wina, ayenera kupitirira kumpatsa woyambayo chakudya ndi zovala. Azimlolanso zonse zomuyenera ngati mkazi wake, monga ankachitira kale.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati akwatira mkazi wina, asamumane woyambayo chakudya ngakhale chovala ndipo apiritirize kugona naye ngati mkazi wake.

Onani mutuwo



Eksodo 21:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.


Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana aakazi.