Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 2:1 - Buku Lopatulika

Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu wina wa fuko la Levi adakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo munthu wina wa fuko la Levi anakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo



Eksodo 2:1
6 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Hadadi uja anathawa, iyeyo ndi a ku Edomu ena, akapolo a atate wake pamodzi naye, kunka ku Ejipito, Hadadiyo akali mwana.


Ndipo dzina lake la mkazi wake wa Amuramu ndiye Yokebede, mwana wamkazi wa Levi, wobadwira Levi mu Ejipito; ndipo iye anambalira Amuramu, Aroni ndi Mose, ndi Miriyamu mlongo wao.