Tsopano, umbwezere munthuyo mkazi wake; chifukwa iye ndiye mneneri, ndipo adzakupempherera iwe, ndipo udzakhala ndi moyo: koma ukaleka kumbwezera, udziwe kuti udzafa ndithu, iwe ndi onse amene uli nao.
Eksodo 18:17 - Buku Lopatulika Koma mpongozi wa Mose ananena naye, Chinthu uchitachi sichili chabwino ai. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Koma mpongozi wa Mose ananena naye, Chinthu uchitachi sichili chabwino ai. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Apo Yetero mpongozi wa Moseyo adati, “Simukuchita bwino ai. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mpongozi wa Mose anayankha kuti, “Zimene mukuchitazi si zabwino. |
Tsopano, umbwezere munthuyo mkazi wake; chifukwa iye ndiye mneneri, ndipo adzakupempherera iwe, ndipo udzakhala ndi moyo: koma ukaleka kumbwezera, udziwe kuti udzafa ndithu, iwe ndi onse amene uli nao.
akakhala nao mlandu adza kwa ine, kuti ndiweruze pakati pa munthu ndi mnansi wake, ndi kuti ndiwadziwitse malemba a Mulungu, ndi malamulo ake.
Udzalema konse, iwe ndi anthu amene uli nao; pakuti chikukanika chinthu ichi; sungathe kuchichita pa wekha.
Mafuta ndi zonunkhira zikondweretsa mtima, ndi ubwino wa bwenzi uteronso pakupangira uphungu.
Ndipo khumi ndi awiriwo anaitana unyinji wa ophunzira, nati, Sikuyenera kuti ife tisiye kulalikira mau a Mulungu ndi kutumikira podyerapo.