Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 18:17 - Buku Lopatulika

Koma mpongozi wa Mose ananena naye, Chinthu uchitachi sichili chabwino ai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma mpongozi wa Mose ananena naye, Chinthu uchitachi sichili chabwino ai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Yetero mpongozi wa Moseyo adati, “Simukuchita bwino ai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mpongozi wa Mose anayankha kuti, “Zimene mukuchitazi si zabwino.

Onani mutuwo



Eksodo 18:17
5 Mawu Ofanana  

Tsopano, umbwezere munthuyo mkazi wake; chifukwa iye ndiye mneneri, ndipo adzakupempherera iwe, ndipo udzakhala ndi moyo: koma ukaleka kumbwezera, udziwe kuti udzafa ndithu, iwe ndi onse amene uli nao.


akakhala nao mlandu adza kwa ine, kuti ndiweruze pakati pa munthu ndi mnansi wake, ndi kuti ndiwadziwitse malemba a Mulungu, ndi malamulo ake.


Udzalema konse, iwe ndi anthu amene uli nao; pakuti chikukanika chinthu ichi; sungathe kuchichita pa wekha.


Mafuta ndi zonunkhira zikondweretsa mtima, ndi ubwino wa bwenzi uteronso pakupangira uphungu.


Ndipo khumi ndi awiriwo anaitana unyinji wa ophunzira, nati, Sikuyenera kuti ife tisiye kulalikira mau a Mulungu ndi kutumikira podyerapo.