Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:13 - Buku Lopatulika

Ndipo kunali madzulo zinakwera zinziri, ndipo zinakuta tsasa, ndi m'mawa padagwa mame pozungulira tsasa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo kunali madzulo zinakwera zinziri, ndipo zinakuta tsasa, ndi m'mawa padagwa mame pozungulira tsasa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero madzulo kudagwa zinziri, ndipo zidadzaza ponseponse pamahemapo. M'maŵa ndithu padagwa mame ponse pozungulira mahemawo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Madzulo amenewo panatuluka zinziri zimene zinali ponseponse pa misasa yawo, ndipo mmawa panali mame kuzungulira misasa yawo.

Onani mutuwo



Eksodo 16:13
4 Mawu Ofanana  

Anafunsa ndipo Iye anadzetsa zinziri, nawakhutitsa mkate wakumwamba.


Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.