Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 14:6 - Buku Lopatulika

Ndipo anamanga galeta lake, napita nao anthu ake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamanga galeta lake, napita nao anthu ake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Farao adakonzetsa galeta lake lankhondo, ndipo adauza asilikali ake kuti apite naye limodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho anakonzetsa galeta lake ndipo ananyamuka pamodzi ndi ankhondo ake.

Onani mutuwo



Eksodo 14:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anauza mfumu ya Aejipito kuti anthu adathawa; ndi mtima wa Farao ndi wa anyamata ake inasandulikira anthuwo, ndipo anati, Ichi nchiyani tachita, kuti talola Israele amuke osatigwiriranso ntchito?


napita nao magaleta osankhika mazana asanu ndi limodzi, ndi magaleta onse a mu Ejipito, ndi akapitao ao onse.


Magaleta a Farao ndi nkhondo yake anawaponya m'nyanja; ndi akazembe ake osankhika anamira mu Nyanja Yofiira.