Eksodo 14:7 - Buku Lopatulika7 napita nao magaleta osankhika mazana asanu ndi limodzi, ndi magaleta onse a mu Ejipito, ndi akapitao ao onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 napita nao magaleta osankhika mazana asanu ndi limodzi, ndi magaleta onse a m'Ejipito, ndi akapitao ao onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adatenga magaleta amphamvu 600 pamodzi ndi magaleta ena onse ndipo adaika atsogoleri pa magaleta onsewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye anatenga magaleta 600 abwino kwambiri pamodzi ndi magaleta ena a dziko la Igupto. Anatenganso akuluakulu onse ankhondo. Onani mutuwo |