Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 13:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauzanso Mose kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo



Eksodo 13:1
4 Mawu Ofanana  

Ndipo kunakhala tsiku lomwelo, kuti Yehova anatulutsa ana a Israele m'dziko la Ejipito, monga mwa makamu ao.


kuti uzikapatulira Yehova onse oyamba kubadwa ndi oyamba onse uli nao odzera kwa zoweta; amunawo ndi a Yehova.


Ndipatulire Ine yense woyamba kubadwa, wotsegulira pa amake mwa ana a Israele, mwa anthu ndi mwa zoweta; ndiwo anga.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,