Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 13:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauzanso Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 13:1
4 Mawu Ofanana  

Ndipo tsiku lomwelo Yehova anatulutsa gulu lonse la ana a Israeli mʼdziko la Igupto.”


muzikapereka kwa Ambuye ana onse oyamba kubadwa. Ziweto zonse zazimuna zoyamba kubadwa ndi za Ambuye.


“Ana onse aamuna oyamba kubadwa uwapatule, ndi anga. Aliyense woyamba kubadwa pakati pa Aisraeli ndi wanga, kaya ndi wa munthu kapena wa chiweto.”


Kenaka Yehova anati kwa Mose,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa