Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 12:44 - Buku Lopatulika

koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kapolo aliyense wochita kugulidwa angadyeko, koma atayamba waumbalidwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kapolo aliyense amene munagula angadye ngati atayamba wachita mdulidwe.

Onani mutuwo



Eksodo 12:44
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anatenga Ismaele mwana wake ndi onse amene anabadwa m'nyumba mwake, ndi onse amene anagulidwa ndi ndalama zake, amuna onse a mwa anthu a kunyumba kwake kwa Abrahamu, nadula khungu lao tsiku lomwelo, monga Mulungu ananena naye.


Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.