Ndipo Abrahamu anatenga Ismaele mwana wake ndi onse amene anabadwa m'nyumba mwake, ndi onse amene anagulidwa ndi ndalama zake, amuna onse a mwa anthu a kunyumba kwake kwa Abrahamu, nadula khungu lao tsiku lomwelo, monga Mulungu ananena naye.
Eksodo 12:44 - Buku Lopatulika koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Kapolo aliyense wochita kugulidwa angadyeko, koma atayamba waumbalidwa. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Kapolo aliyense amene munagula angadye ngati atayamba wachita mdulidwe. |
Ndipo Abrahamu anatenga Ismaele mwana wake ndi onse amene anabadwa m'nyumba mwake, ndi onse amene anagulidwa ndi ndalama zake, amuna onse a mwa anthu a kunyumba kwake kwa Abrahamu, nadula khungu lao tsiku lomwelo, monga Mulungu ananena naye.
Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.