Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 22:11 - Buku Lopatulika

11 Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Koma wansembe akagula kapolo ndi ndalama kuti akhale wake, kapoloyo angathe kudya nao zinthuzo. Ndipo onse amene abadwa m'nyumba mwa wansembe angathe kudyako chakudya chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Koma kapolo amene wagulidwa ndi ndalama kapena kubadwira mʼbanja la wansembe angathe kudya chakudya cha wansembeyo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 22:11
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anatenga Sarai mkazi wake, ndi Loti mwana wa mphwake, ndi chuma chao chimene anasonkhanitsa, ndi miyoyo imene anabala mu Harani; natuluka kunka ku dziko la Kanani, ndipo anadza ku dziko la Kanani.


Azidulidwatu amene abadwa m'nyumba mwako ndi amene agulidwa ndi ndalama zako: ndipo pangano langa lidzakhala m'thupi mwako pangano losatha.


koma kapolo wa mwini aliyense, wogula ndi ndalama, utamdula, ndipo adyeko.


Adye chakudya cha Mulungu wake, chopatulika kwambiri, ndi chopatulika;


Ndipo mwana wamkazi wa wansembe akakwatibwa ndi mlendo, asadyeko nsembe yokweza ya zinthu zopatulika.


Izi ndi zako pa zinthu zopatulika kwambiri, zosafika kumoto; zopereka zao zonse, ndi nsembe zao zonse zaufa, ndi nsembe zao zonse zauchimo, ndi nsembe zao zonse zopalamula, zimene andibwezera Ine, zikhale zopatulika kwambiri za iwe ndi za ana ako aamuna.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa