Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 1:13 - Buku Lopatulika

Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo mupenye maonekedwe athu ndi maonekedwe a anyamata akudya chakudya cha mfumu; ndi monga umo muonera, muchitire anyamata anu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mudzafananize maonekedwe athu ndi a anyamata amene akudya chakudya cha mfumu, ndi kuti mudzachite ndi anyamata anu monga momwe mudzawaonere.”

Onani mutuwo



Danieli 1:13
2 Mawu Ofanana  

Muyesetu anyamata anu masiku khumi; atipatse zomera m'nthaka tidye, ndi madzi timwe.


Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.