Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Amosi 3:3 - Buku Lopatulika

Kodi awiri adzayenda pamodzi asanapanganiranetu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi awiri adzayenda pamodzi asanapanganiranetu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Kodi anthu aŵiri nkuyendera pamodzi, osapangana?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi anthu awiri nʼkuyendera limodzi asanapangane?

Onani mutuwo



Amosi 3:3
7 Mawu Ofanana  

Pamene Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, Yehova anamuonekera Abramu nati kwa iye, Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse; yenda iwe pamaso panga, nukhale wangwiro.


ndipo Enoki anayendabe ndi Mulungu, atabala Metusela, zaka mazana atatu, nabala ana aamuna ndi aakazi;


Mibadwo ya Nowa ndi iyi: Nowa anali munthu wolungama ndi wangwiro m'mibadwo yake; Nowa anayendabe ndi Mulungu.


Inu nokha ndinakudziwani mwa mabanja onse a padziko lapansi, m'mwemo ndidzakulangani chifukwa cha mphulupulu zanu zonse.


Kodi mkango udzabangula m'nkhalango wosakhala nayo nyama? Kodi msona wa mkango udzalira m'ngaka mwake usanagwire kanthu?


Tamverani mau awa, inu ng'ombe zazikazi za ku Basani, zokhala m'phiri la Samariya, zosautsa aumphawi, zopsinja osowa, zonena kwa ambuyao, Bwerani nacho, timwe.