Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 2:24 - Buku Lopatulika

koma ndikhulupirira mwa Ambuye kuti ine ndekhanso ndidzadza msanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma ndikhulupirira mwa Ambuye kuti ine ndekhanso ndidzadza msanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ndikhulupirira kuti, Ambuye akalola, inenso ndidzafika kwanuko msanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ndikukhulupirira kuti Ambuye akalola ine mwini ndidzafikanso kwanuko posachedwapa.

Onani mutuwo



Afilipi 2:24
6 Mawu Ofanana  

Koma ndiyembekeza mwa Ambuye Yesu kuti ndidzatumiza Timoteo kwa inu msanga, kuti inenso nditonthozeke bwino pozindikira za kwa inu.


Koma undikonzerenso pogona; pakuti ndiyembekeza kuti mwa mapemphero anu ndidzapatsidwa kwa inu.


Pokhala ndili nazo zambiri zakukulemberani, sindifuna kuchita ndi kalata ndi kapezi; koma ndiyembekeza kudza kwa inu, ndi kulankhula popenyana, kuti chimwemwe chanu chikwanire.


koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana.