Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 17:26 - Buku Lopatulika

Ndipo Israele ndi Abisalomu anamanga zithando m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Israele ndi Abisalomu anamanga zithando m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Aisraele pamodzi ndi Abisalomu adamanga zithando zankhondo m'dziko la Giliyadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli ndi Abisalomu anamanga zithando mʼdziko la Giliyadi.

Onani mutuwo



2 Samueli 17:26
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Abisalomu anaika Amasa, kazembe wa khamulo, m'malo a Yowabu. Koma Amasayu ndiye mwana wa munthu dzina lake Yetere Mwismaele, amene analowa kwa Abigaile, mwana wamkazi wa Nahasi, mlongo wa Zeruya, amai a Yowabu.


Ndipo kunali pakufika Davide ku Mahanaimu, Sobi mwana wa Nahasi wa ku Raba wa ana a Amoni, ndi Makiri mwana wa Amiyele wa ku Lodebara, ndi Barizilai Mgiliyadi wa ku Rogelimu,


Chomwecho anthuwo anatulukira kuthengo kukamenyana ndi Israele; nalimbana ku nkhalango ya ku Efuremu.


Ndipo ndinampatsa Makiri Giliyadi.


Gawo la fuko la Manase ndi ili: pakuti anali woyamba wa Yosefe. Makiri mwana woyamba wa Manase, atate wa Giliyadi, popeza ndiye munthu wa nkhondo, anakhala nayo Giliyadi ndi Basani.