Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 17:13 - Buku Lopatulika

Ndiponso ngati walowa kumzinda wina, Aisraele onse adzabwera ndi zingwe kumzindako, ndipo tidzaukokera kumtsinje, kufikira sikapezeka kamwala kakang'ono kumeneko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndiponso ngati walowa kumudzi wina, Aisraele onse adzabwera ndi zingwe kumudziko, ndipo tidzaukokera kumtsinje, kufikira sikapezeka kamwala kakang'ono kumeneko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akakaloŵa mumzinda mwina, Aisraele onse adzabwera ndi zingwe kumzindako. Mzinda umenewo tidzauguzira ku chigwa, ndipo sipadzapezeka ndi kamwala komwe kumeneko.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye akakathawira mu mzinda, Aisraeli onse adzabweretsa zingwe ku mzindawo, ndipo ife tidzawugwetsera ku chigwa mpaka sipadzapezeka ngakhale kachidutswa.”

Onani mutuwo



2 Samueli 17:13
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Abisalomu ndi anthu onse a Israele anati, Uphungu wa Husai Mwariki uposa uphungu wa Ahitofele. Pakuti kunaikidwa ndi Yehova kutsutsa uphungu wabwino wa Ahitofele kuti Yehova akamtengere Abisalomu choipa.


Chifukwa chake ndidzaika Samariya ngati mulu wa miyala ya m'munda, ngati zooka m'munda wampesa; ndipo ndidzataya miyala yake m'chigwa, ndi kufukula maziko ake.


Koma Iye anayankha nati kwa iwo, Simuona izi zonse kodi? Indetu ndinena kwa inu, Sipadzakhala pano mwala umodzi pa unzake, umene sudzagwetsedwa.