Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 7:16 - Buku Lopatulika

Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikukondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndine wokondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.

Onani mutuwo



2 Akorinto 7:16
5 Mawu Ofanana  

nulimbika mumtima kuti iwe wekha uli wotsogolera wa akhungu, nyali ya amene akhala mumdima,


Ndipo ndinalemba ichi chomwe, kuti pakudza ndisakhale nacho chisoni kwa iwo amene ayenera kukondweretsa ine; ndi kukhulupirira mwa inu nonse, kuti chimwemwe changa ndi chanu cha inu nonse.


koma tikhulupirira mwa Ambuye za inu, kuti mumachita, ndiponso mudzachita zimene tikulamulirani.


Pokhulupirira kumvera kwako ndikulembera iwe, podziwa kuti udzachitanso koposa chimene ndinena.


Momwemo, ndingakhale ndili nako kulimbika mtima kwakukulu mu Khristu kukulamulira chimene chiyenera,