Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 5:3 - Buku Lopatulika

ngatitu povekedwa sitidzapezedwa amaliseche.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ngatitu povekedwa sitidzapezedwa amaliseche.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kuti titaivala, tisadzapezeke amaliseche.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

chifukwa tikavala, sitidzapezekanso amaliseche.

Onani mutuwo



2 Akorinto 5:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Mose anaona kuti anthu anamasuka, popeza Aroni adawamasula kuti awatonze adani ao,


Pakutinso m'menemo tibuula, ndi kukhumbitsa kuvekedwa ndi chokhalamo chathu chochokera Kumwamba;


Pakutinso ife okhala mu msasawu tibuula, pothodwa; si kunena kuti tifuna kuvulidwa, koma kuvekedwa, kuti chaimfacho chimezedwe ndi moyo.


(Taonani, ndidza ngati mbala. Wodala iye amene adikira, nasunga zovala zake, kuti angayende wausiwa, nangapenye anthu usiwa wake.)


ndikulangiza ugule kwa Ine golide woyengeka m'moto, kuti ukakhale wachuma, ndi zovala zoyera, kuti ukadziveke, ndi kuti manyazi a usiwa wako asaoneke; ndi mankhwala opaka m'maso mwako, kuti ukaone.