Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 2:6 - Buku Lopatulika

Kwa wotereyo chilango ichi chidachitika ndi ambiri chikwanira;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kwa wotereyo chilango ichi chidachitika ndi ambiri chikwanira;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu woteroyo, pafupi nonse mwamtsutsa, choncho chilangocho nchokwanira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chilango chimene ambiri a inu mwamupatsa munthu ameneyu nʼchokwanira.

Onani mutuwo



2 Akorinto 2:6
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa cha ichi ndilembera izi pokhala palibe ine, kuti pokhala ndili pomwepo ndingachite mowawitsa, monga mwa ulamuliro umene Ambuye anandipatsa ine wakumangirira, ndipo si wakugwetsa.


Pakuti, taonani, ichi chomwe, chakuti mudamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, khama lalikulu lanji chidalichita mwa inu, komanso chodzikonza, komanso mkwiyo, komanso mantha, komanso kukhumbitsa komanso changu, komanso kubwezera chilango! M'zonse munadzitsimikizira nokha kuti muli oyera mtima m'menemo.


Iwo akuchimwa uwadzudzule pamaso pa onse, kuti otsalawo achite mantha.