Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 13:12 - Buku Lopatulika

Mupatsane moni ndi kupsompsonana kopatulika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mupatsane moni ndi chipsompsono chopatulika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mupatsane moni mwa chikondi choona.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Lonjeranani ndi mpsopsono wachiyero.

Onani mutuwo



2 Akorinto 13:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Mupatsane moni wina ndi mnzake ndi kupsompsonana kopatulika. Mipingo yonse ya Khristu ikupatsani moni.


Akupatsani moni abale onse. Mupatsane moni ndi kupsompsonana kopatulika.


Perekani moni kwa abale onse ndi chipsompsono chopatulika.


Mupatsane moni ndi kupsompsonana kwa chikondi. Mtendere ukhale ndi inu nonse muli mwa Khristu.