Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Akorinto 13:13 - Buku Lopatulika

13 Oyera mtima onse akupatsani moni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Oyera mtima onse akupatsani moni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Anthu onse a Mulungu akukupatsani moni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Anthu onse a Mulungu akupereka moni.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 13:13
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Mupatsane moni wina ndi mnzake ndi kupsompsonana kopatulika. Mipingo yonse ya Khristu ikupatsani moni.


Perekani moni kwa atsogoleri anu onse, ndi oyera mtima onse. Akupatsani moni iwo a ku Italiya.


Iye wa ku Babiloni wosankhidwa pamodzi nanu akukupatsani moni; ateronso Marko mwana wanga.


Akupereka moni ana a mbale wanu wosankhika.


koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa