Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 26:4 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake Davide anatumiza ozonda, nazindikira kuti Saulo anabwera ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake Davide anatumiza ozonda, nazindikira kuti Saulo anabwera ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Davide adatuma anthu oti akazonde, ndipo adapezadi kuti Saulo wafika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

iye anatumiza anthu okazonda ndipo anapeza kuti Sauli wafikadi ndithu.

Onani mutuwo



1 Samueli 26:4
4 Mawu Ofanana  

Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, ali ku Sitimu, anatuma amuna awiri mosadziwika kukazonda, ndi kuti, Mukani, mulipenye dzikolo, ndi ku Yeriko. Ndipo anamuka nalowa m'nyumba ya mkazi wadama, dzina lake Rahabi, nagona momwemo.


Saulo namanga zithando m'phiri la Hakila kupenya kuchipululu kunjira. Koma Davide anakhala kuchipululu, naona kuti Saulo alikumfuna kuchipululu komweko.


Ndipo Davide ananyamuka nafika pamalo paja Saulo anamangapo; ndipo Davide adaona pogona Saulo, ndi Abinere mwana wa Nere kazembe wa khamu lake; ndipo Saulo anagona pakati pa linga la magaleta, ndipo anthu adamanga zithando pomzinga pake.