1 Samueli 26:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 iye anatumiza anthu okazonda ndipo anapeza kuti Sauli wafikadi ndithu. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Chifukwa chake Davide anatumiza ozonda, nazindikira kuti Saulo anabwera ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chifukwa chake Davide anatumiza ozonda, nazindikira kuti Saulo anabwera ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Davide adatuma anthu oti akazonde, ndipo adapezadi kuti Saulo wafika. Onani mutuwo |