Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 13:23 - Buku Lopatulika

Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Afilisti adatuma kagulu kankhondo kukalonda mpata wa Mikimasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono gulu lina lankhondo la Chifilisti linapita kukalonda mpata wa Mikimasi.

Onani mutuwo



1 Samueli 13:23
7 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide anali m'linga, ndi boma la Afilisti linali mu Betelehemu.


Wafika ku Ayati, wapitirira kunka ku Migironi; pa Mikimasi asunga akatundu ake;


wapita pampata; wagona pa Geba, Rama anthunthumira; Gibea wa Saulo wathawa.


Ndipo Afilisti anasonkhana kuti akamenyane ndi Aisraele, anali nao magaleta zikwi makumi atatu, ndi apakavalo zikwi zisanu ndi chimodzi, ndi anthu akuchuluka monga mchenga wa m'mphepete mwa nyanja. Iwowa anakwera namanga zithando ku Mikimasi kum'mawa kwa Betaveni.


Ndipo kunali tsiku lina kuti Yonatani mwana wa Saulo ananena ndi mnyamata wonyamula zida zake, Tiye tipite kunka ku kaboma ka Afilisti, tsidya lija. Koma sanauze atate wake.