Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 1:25 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anapha ng'ombe, nabwera naye mwanayo kwa Eli.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anapha ng'ombe, nabwera naye mwanayo kwa Eli.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumeneko adapha ng'ombe yamphongo ija ndipo mwanayo adampereka kwa Eli.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono anapha ngʼombe yamphongo ija ndi kupereka mwana uja kwa Eli.

Onani mutuwo



1 Samueli 1:25
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo aiphe ng'ombeyo pamaso pa Yehova; ndipo ana a Aroni, ansembewo, abwere nao mwazi, nawaze mwaziwo pozungulira paguwa la nsembe, lokhala pa khoma la chihema chokomanako.


Ndipo pamene anakwanira masiku a kukonza kwao, monga mwa chilamulo cha Mose, iwo anakwera naye kunka ku Yerusalemu, kukamsonyeza Iye kwa Ambuye,