Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 3:2 - Buku Lopatulika

Ndinadyetsa inu mkaka, si chakudya cholimba ai; pakuti simungachithe; ngakhale tsopano lino simungachithe; pakuti mulinso athupi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinadyetsa inu mkaka, si chakudya cholimba ai; pakuti simunachikhoza; ngakhale tsopano lino simuchikhoza; pakuti mulinso athupi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndidakumwetsani mkaka, osakupatsani chakudya cholimba, chifukwa simukadatha kuchidya. Ngakhalenso tsopano simungathe kuchidya,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe.

Onani mutuwo



1 Akorinto 3:2
3 Mawu Ofanana  

Ndili nazo zambirinso zakunena kwa inu, koma simungathe kuzisenza tsopano lino.


lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda chinyengo, kuti mukakule nao kufikira chipulumutso;