1 Petro 2:2 - Buku Lopatulika2 lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda chinyengo, kuti mukakule nao kufikira chipulumutso; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda chinyengo, kuti mukakule nao kufikira chipulumutso; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Monga makanda obadwa chatsopano amalirira mkaka, inunso muzilakalaka mkaka weniweni wodyetsa mtima wanu, kuti ukukuzeni ndi kukufikitsani ku chipulumutso, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Monga makanda obadwa kumene amalirira mkaka, inunso muzilakalaka mkaka weniweni wauzimu, kuti mukule ndi kukufikitsani ku chipulumutso chanu, Onani mutuwo |