Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 16:3 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene ndifika, ndidzatuma iwo amene mudzawayesa oyenera, ndi makalata, apite nayo mphatso yanu ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene ndifika, ndidzatuma iwo amene mudzawayesa oyenera, ndi akalata, apite nayo mphatso yanu ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ndikadzafika, ndidzaŵapatsa makalata anthu amene mungaŵasankhe, ndipo ndidzaŵatuma kuti akapereke mphatso yanuyo ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo, ndikadzafika, ndidzawapatsa makalata a umboni anthu amene mudzawasankhe ndi kuwatuma kuti akapereka mphatso zanu ku Yerusalemu.

Onani mutuwo



1 Akorinto 16:3
8 Mawu Ofanana  

Ngati wina ali ndi njala adye kwao; kuti mungasonkhanire kwa chiweruziro. Koma zotsalazo ndidzafotokoza pakudza ine.


Ndipo ngati kuyenera kwa ine kupitanso, adzapita nane.


Kodi tilikuyambanso kudzivomereza tokha? Kapena kodi tisowa, monga ena, makalata otivomerezetsa kwa inu, kapena ochokera kwa inu?


anachita eni ake, natiumiriza ndi kutidandaulira za chisomocho, ndi za chiyanjano cha utumiki wa kwa oyera mtima;


Kotero kuti tinadandaulira Tito, kuti monga anayamba kale, chomwechonso atsirize kwa inu chisomo ichinso.