Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 74,600.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ao, ndiwo zikwi makumi asanu ndi awiri, mphambu zinai, kudza mazana asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo khamu lake, ndi owerengedwa ao, ndiwo zikwi makumi asanu ndi awiri, mphambu zinai, kudza mazana asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 ndipo ankhondo ake ngokwanira 74,600.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:4
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Yuda chinali 74, 600.


Kummawa, kotulukira dzuwa, magulu a msasa wa Yuda amange pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Ayudawo ndi Naasoni mwana wa Aminadabu.


Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.


Awa ndiwo anali mafuko a Yuda. Amene anawerenga analipo 76,500.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa