Numeri 13:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Monga mwa mawu a Yehova, Mose anawatuma kuchokera ku chipululu cha Parani. Onsewo anali atsogoleri a Aisraeli. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo Mose anawatumiza kuchokera ku chipululu cha Parani monga mwa mau a Yehova; amuna onsewa ndiwo akulu a ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Mose anawatumiza kuchokera ku chipululu cha Parani monga mwa mau a Yehova; amuna onsewa ndiwo akulu a ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Choncho Mose adaŵatuma kuchokera ku chipululu cha Parani, monga momwe Chauta adaalamulira, ndipo onsewo anali atsogoleri a Aisraele. Onani mutuwo |