Numeri 13:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mayina awo ndi awa: kuchokera ku fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri; Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Maina ao ndi aŵa: m'fuko la Rubeni, adatuma Samuwa mwana wa Zakuri. Onani mutuwo |
“Nawa mayina a mafuko a Israeli: Dani adzakhala ndi chigawo chimodzi kuyambira kumalire akumpoto kuchokera ku nyanja kudzera ku Hetiloni mpaka ku chipata cha Hamati, kukafika ku Hazari-Enani, mzinda umene uli kumpoto kwa malire a Damasiko oyangʼanana ndi Hamati, kuchokera mʼchigawo chimodzi kummawa mpaka kumadzulo.