Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 13:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mayina awo ndi awa: kuchokera ku fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Maina ao ndi aŵa: m'fuko la Rubeni, adatuma Samuwa mwana wa Zakuri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:4
10 Mawu Ofanana  

Israeli akanali mʼderali, Rubeni anapita nakagonana ndi Biliha, mdzakazi wa abambo ake. Yakobo uja anazimva zimenezi. Yakobo anali ndi ana aamuna khumi ndi awiri:


Ana a Leya ndi awa: Rubeni anali mwana woyamba wa Yakobo, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, ndi Zebuloni.


Ana a Israeli anali awa: Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni,


“Nawa mayina a mafuko a Israeli: Dani adzakhala ndi chigawo chimodzi kuyambira kumalire akumpoto kuchokera ku nyanja kudzera ku Hetiloni mpaka ku chipata cha Hamati, kukafika ku Hazari-Enani, mzinda umene uli kumpoto kwa malire a Damasiko oyangʼanana ndi Hamati, kuchokera mʼchigawo chimodzi kummawa mpaka kumadzulo.


Monga mwa mawu a Yehova, Mose anawatuma kuchokera ku chipululu cha Parani. Onsewo anali atsogoleri a Aisraeli.


kuchokera ku fuko la Simeoni, Safati mwana wa Hori;


Ndipo anthu amene Mose anawatuma kukazonda dziko aja anachoka pamaso pake nachititsa gulu lonse la anthu kuwukira Moseyo chifukwa chofalitsa mbiri yoyipa ya dzikolo.


Chifukwa chiyani mukufowoketsa Aisraeli kupita mʼdziko limene Yehova wawapatsa?


Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda,


Ochokera fuko la Yuda analipo 12,000 amene analembedwa chizindikiro. Ochokera fuko la Rubeni analipo 12,000; ochokera fuko la Gadi analipo 12,000;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa