Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 11:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Motero malowo anawatcha Tabera, chifukwa moto wa Yehova unayaka pakati pawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndipo anatcha malowo dzina lake Tabera; popeza moto wa Yehova udayaka pakati pao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anatcha malowo dzina lake Tabera; popeza moto wa Yehova udayaka pakati pao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Motero malowo adaŵatcha Tabera, chifukwa choti moto wa Chauta udayaka pakati pao.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:3
4 Mawu Ofanana  

Yehova atawamva anakwiya kwambiri; moto wake unayaka kutsutsana ndi Yakobo, ndipo mkwiyo wake unauka kutsutsana ndi Israeli,


Anthu ena osokoneza amene anali pakati pa Aisraeli anayamba kukhumba chakudya cha ku Igupto ndipo Aisraeli nawonso anayamba kufuwula kwambiri nʼkumati, “Tikanangopeza nyama yoti nʼkudya!


Ndipo moto wochokera kwa Yehova unabwera nʼkunyeketsa anthu 250 amene ankapereka nsembe yofukiza aja.


Inu munamukwiyitsanso Yehova ku Tabera, ku Masa ndi ku Kibiroti Hatava.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa