Filemoni 1:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kwa Apiya mlongo wathu, Arkipo msilikali mnzathu, ndiponso mpingo umene umasonkhana mʼnyumba mwanu. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 ndi kwa Afiya mlongoyo, ndi Arkipo msilikali mnzathu, ndi kwa Mpingo uli m'nyumba yako: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndi kwa Afiya mlongoyo, ndi Arkipo msilikali mnzathu, ndi kwa Mpingo uli m'nyumba yako: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kalata yomweyinso tikulembera Afiya, mlongo wathu, ndi Arkipo, msilikali mnzathu pa nkhondo ya Mulungu, ndiponso mpingo wonse umene umasonkhana kunyumba kwanu. Onani mutuwo |