Eksodo 3:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono Mose anati mu mtima mwake, “Ine ndipita komweko ndikaone zodabwitsazi, chitsamba sichikunyeka chifukwa chiyani?” Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo Mose anati, Ndipatuketu, ndikaone chooneka chachikulucho, chitsambacho sichinyeka bwanji. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Mose anati, Ndipatuketu, ndikaone chooneka chachikulucho, chitsambacho sichinyeka bwanji. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono mumtima mwake adati, “Ndipita pafupi, kuti ndikaonetsetse zozizwitsa ndikupenyazi. Chifukwa chiyani chitsambacho sichilikupsa?” Onani mutuwo |