Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 3:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo Mose anati, Ndipatuketu, ndikaone chooneka chachikulucho, chitsambacho sichinyeka bwanji.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo Mose anati, Ndipatuketu, ndikaone chooneka chachikulucho, chitsambacho sichinyeka bwanji.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Tsono mumtima mwake adati, “Ndipita pafupi, kuti ndikaonetsetse zozizwitsa ndikupenyazi. Chifukwa chiyani chitsambacho sichilikupsa?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Tsono Mose anati mu mtima mwake, “Ine ndipita komweko ndikaone zodabwitsazi, chitsamba sichikunyeka chifukwa chiyani?”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 3:3
5 Mawu Ofanana  

Tamverani ichi, Yobu. Taimani, mulingirire zodabwitsa za Mulungu.


Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu!


Ndipo mthenga wa Yehova anamuonekera m'chilangali chamoto chotuluka m'kati mwa chitsamba; ndipo anapenya, ndipo taonani, chitsamba chilikuyaka moto, koma chosanyeka chitsambacho.


Koma Mose pakuona, anazizwa pa choonekacho; ndipo pakuyandikira iye kukaona, kunadza mau a Ambuye,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa