Danieli 11:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka mfumu yamphamvu idzafika imene idzalamulira ndi ufumu waukulu ndi kuchita zimene ifuna. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo idzauka mfumu yamphamvu, nidzachita ufumu ndi ulamuliro waukulu, nidzachita monga mwa chifuniro chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo idzauka mfumu yamphamvu, nidzachita ufumu ndi ulamuliro waukulu, nidzachita monga mwa chifuniro chake. Onani mutuwo |